1 Samueli 8:8 - Buku Lopatulika8 Monga ntchito zao zonse anazichita kuyambira tsiku lija ndinawatulutsa ku Ejipito, kufikira lero lino kuti anandisiya Ine, natumikira milungu ina, momwemo alikutero ndi iwenso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Monga ntchito zao zonse anazichita kuyambira tsiku lija ndinawatulutsa ku Ejipito, kufikira lero lino kuti anandisiya Ine, natumikira milungu ina, momwemo alikutero ndi iwenso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Kuyambira tsiku limene ndidaŵatulutsa ku Ejipito mpaka pano, zochita zao nzokhazokha za kundikana ine ndi kutumikira milungu ina. Tsono nawenso akukuchita zomwezo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Kuyambira tsiku limene ndinawatulutsa mʼdziko la Igupto mpaka lero zochita zawo zakhala zondikana Ine nʼkumatumikira milungu ina. Tsopano akukukananso iwe. Onani mutuwo |