1 Samueli 8:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo Yehova ananena ndi Samuele, Umvere mau onse anthuwo alikulankhula nawe; popeza sindiwe anakukana, koma ndine anandikana, kuti ndisakhale mfumu yao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo Yehova ananena ndi Samuele, Umvere mau onse anthuwo alikulankhula nawe; popeza sindiwe anakukana, koma ndine anandikana, kuti ndisakhale mfumu yao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Apo Chauta adayankha kuti, “Umvere zonse zimene anthuwo akukuuza. Sakukana iwe koma Ine. Sakufuna kuti ndikhale mfumu yao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Yehova anamuyankha nati, “Mvera zonse zimene anthuwa akukuwuza. Si ndiwe amene akumukana, koma akukana Ine kuti ndikhale mfumu yawo. Onani mutuwo |