1 Samueli 8:6 - Buku Lopatulika6 Koma chimenechi sichinakondweretse Samuele, pamene iwo anati, Tipatseni mfumu kuti itiweruze. Ndipo Samuele anapemphera kwa Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Koma chimenechi sichinakondweretsa Samuele, pamene iwo anati, Tipatseni mfumu kuti itiweruze. Ndipo Samuele anapemphera kwa Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Mau ameneŵa akuti “Mutipatse mfumu yoti izitilamulira” sadamkondwetse Samuele. Nchifukwa chake Samueleyo adapemphera kwa Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Koma mawu oti, “Mutipatse mfumu kuti izitilamulira,” sanakondweretse Samueli. Choncho anapemphera kwa Yehova. Onani mutuwo |