1 Samueli 8:20 - Buku Lopatulika20 kuti ifenso tikafanane nao anthu a mitundu yonse; kuti mfumu yathuyo ikatiweruzire, ndi kutuluka kutitsogolera, ndi kuponya nafe nkhondo zathu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 kuti ifenso tikafanane nao anthu a mitundu yonse; kuti mfumu yathuyo ikatiweruzire, ndi kutuluka kutitsogolera, ndi kuponya nafe nkhondo zathu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Tikufuna kuti nafenso tikhale ngati mitundu ina yonse, ndipo kuti mfumu yathu izitiweruza, kutitsogolera ndi kumatimenyera nkhondo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Kotero ifenso tidzakhala ngati mayiko ena. Mfumu yathu idzatiweruza ndiponso idzatuluka nafe kutitsogolera kukamenya nkhondo.” Onani mutuwo |