1 Samueli 8:19 - Buku Lopatulika19 Koma anthu anakana kumvera mau a Samuele; nati, Iai, koma tifuna kukhala nayo mfumu yathu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Koma anthu anakana kumvera mau a Samuele; nati, Iai, koma tifuna kukhala nayo mfumu yathu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Koma anthuwo adakana kumvera mau a Samuele. Adati, “Iyai! Ife tikufuna mfumu yotilamulira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Koma anthu anakana kumumvera Samueli. Iwo anati, “Ayi! Ife tikufuna mfumu yotilamulira. Onani mutuwo |