Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 8:13 - Buku Lopatulika

13 Ndipo idzatenga ana anu aakazi apange zonunkhira, naphikire, naumbe mikate.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Ndipo idzatenga ana anu akazi apange zonunkhira, naphikire, naumbe mikate.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Izidzatenga ana anu aakazi kuti azidzayenga mafuta onunkhira, ndi kumaphika chakudya ndi kumapanga buledi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Iyo idzatenga ana anu akazi kuti akhale oyenga mafuta onunkhira, ophika chakudya ndi kupanga buledi.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 8:13
2 Mawu Ofanana  

idzawaika akhale otsogolera chikwi, ndi otsogolera makumi asanu; ndipo idzaika ena kulima minda yake, ndi kutema dzinthu zake, ndi kumpangira zipangizo za nkhondo, ndi zipangizo za magaleta.


Ndipo idzalanda minda yanu, ndi minda ya mpesa yanu, ndi minda ya azitona, inde minda yoposayo, nidzaipatsa anyamata ake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa