1 Samueli 8:14 - Buku Lopatulika14 Ndipo idzalanda minda yanu, ndi minda ya mpesa yanu, ndi minda ya azitona, inde minda yoposayo, nidzaipatsa anyamata ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndipo idzalanda minda yanu, ndi minda ya mphesa yanu, ndi minda ya azitona, inde minda yoposayo, nidzaipatsa anyamata ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Idzakulandani minda yanu yabwino kwambiri, minda yanu yamphesa ndi yaolivi, kudzanso minda yanu yazipatso, ndi kuipatsa nduna zake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Idzatenga minda yanu yabwino ya mpesa ndi ya mitengo ya olivi ndipo adzayipereka kwa antchito ake. Onani mutuwo |