1 Samueli 8:11 - Buku Lopatulika11 Nati, Awa ndi makhalidwe a mfumu imene idzaweruza inu; idzatenga ana anu aamuna, akhale akusunga magaleta, ndi akavalo ake; ndipo adzathamanga ndi kutsogolera magaleta ake; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Nati, Awa ndi makhalidwe a mfumu imene idzaweruza inu; idzatenga ana anu amuna, akhale akusunga magaleta, ndi akavalo ake; ndipo adzathamanga ndi kutsogolera magaleta ake; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Adati, “Izi ndizo zimene mfumu yanuyo izidzakuchitani: izidzakulandani ana anu aamuna kuti akhale ankhondo, ena pa magaleta ake ankhondo, ena pa akavalo ake, ndipo ena othamanga patsogolo pa magaletawo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Iye anati, “Zimene mfumu imene idzakulamulireniyo idzachite ndi izi: Izidzatenga ana anu aamuna kuti akhale ankhondo ake; ena pa magaleta ake, ena pa akavalo ake ndipo ena othamanga patsogolo pa magaleta akewo. Onani mutuwo |