Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 8:10 - Buku Lopatulika

10 Ndipo Samuele anauza anthu akumpempha iye mfumu mau onse a Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Ndipo Samuele anauza anthu akumpempha iye mfumu mau onse a Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Choncho Samuele adaŵauza anthu amene ankafuna mfumu aja mau onse a Chauta.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Samueli anawawuza anthu amene amamupempha mfumu aja mawu onse a Yehova.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 8:10
3 Mawu Ofanana  

Ndipo panali pamene Yeremiya anatha kunena kwa anthu onse mau onse a Yehova Mulungu wao, amene anamtuma iye nao Yehova Mulungu wao, mau onse amenewo,


Nati, Awa ndi makhalidwe a mfumu imene idzaweruza inu; idzatenga ana anu aamuna, akhale akusunga magaleta, ndi akavalo ake; ndipo adzathamanga ndi kutsogolera magaleta ake;


Pamenepo akulu onse a Israele anasonkhana, nadza kwa Samuele ku Rama;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa