1 Samueli 6:17 - Buku Lopatulika17 Ndipo amenewa ndiwo mafundo agolide amene Afilisti anabwezera kwa Yehova akhale nsembe yopalamula, kwa Asidodi limodzi, kwa Gaza limodzi, kwa Asikeloni limodzi, kwa Gati limodzi, kwa Ekeroni limodzi; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndipo amenewa ndiwo mafundo agolide amene Afilisti anabwezera kwa Yehova akhale nsembe yopalamula, kwa Asidodi limodzi, kwa Gaza limodzi, kwa Asikeloni limodzi, kwa Gati limodzi, kwa Ekeroni limodzi; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Zifanizo zagolide za mafundo zija zimene Afilisti adapereka ngati nsembe zopepesera Chauta, zinkakhalira mizinda isanu: chimodzi chinali cha ku Asidodi, china cha ku Gaza, china cha ku Asikeloni, china cha ku Gati, china cha ku Ekeroni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Zifanizo zagolide za zithupsa zimene Afilisti anatumiza ngati nsembe zopepesera machimo kwa Yehova zinkayimirira mizinda isanu iyi motere: chimodzi cha ku Asidodi, china cha ku Gaza ndi zina za ku Asikeloni, Gati ndi Ekroni. Onani mutuwo |