1 Samueli 5:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo pamene anthu a ku Asidodi anaona kuti nchomwecho, anati iwowa, Likasa la Mulungu wa Israele lisakhalitse ndi ife; popeza dzanja lake litiwawira ife, ndi Dagoni mulungu wathu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo pamene anthu a ku Asidodi anaona kuti nchomwecho, anati iwowa, Likasa la Mulungu wa Israele lisakhalitse ndi ife; popeza dzanja lake litiwawira ife, ndi Dagoni mulungu wathu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Anthuwo ataona m'mene zinthu zinaliri, adati, “Bokosi lachipangano la Mulungu wa Aisraele lisakhale ndi ife, pakuti Mulungu wao watilanga kwambiri ifeyo ndi mulungu wathu yemwe Dagoni.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Anthu a ku Asidodi ataona zimene zimachitika anati, “Bokosi la Mulungu wa Israeli lisakhale kuno chifukwa akutizunza ife pamodzi ndi mulungu wathu Dagoni.” Onani mutuwo |