1 Samueli 4:5 - Buku Lopatulika5 Pakufika likasalo la chipangano la Yehova kuzithando, Aisraele onse anafuula ndi mau okweza, kotero kuti dziko linachita chivomezi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Pakufika likasalo la chipangano la Yehova kuzithando, Aisraele onse anafuula ndi mau okweza, kotero kuti dziko linachita chivomezi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Pamene Bokosi lachipangano la Chauta lidafika kuzithandoko, Aisraele onse adayamba kufuula kwambiri, kotero kuti nthaka idagwedezeka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Bokosi la Chipangano cha Yehova litafika ku msasa, Aisraeli onse anafuwula kwambiri mpaka nthaka inagwedezeka. Onani mutuwo |