1 Samueli 4:15 - Buku Lopatulika15 Koma Eli anali ndi zaka makumi asanu ndi anai kudza zisanu ndi zitatu; ndipo maso ake anangokhala tong'o osapenya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Koma Eli anali ndi zaka makumi asanu ndi anai kudza zisanu ndi zitatu; ndipo maso ake anangokhala tong'o osapenya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Nthaŵiyo nkuti Eli ali nkhalamba ya zaka 98, maso ake atachita khungu, kotero kuti sankathanso kupenya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Nthawiyo nʼkuti Eli ali wa zaka 98 ndipo maso ake anali atachita khungu kotero kuti samatha kuona. Onani mutuwo |