1 Samueli 4:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo likasa la Mulungu linalandidwa, ndi ana awiri a Eli, Hofeni ndi Finehasi, anaphedwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo likasa la Mulungu linalandidwa, ndi ana awiri a Eli, Hofeni ndi Finehasi, anaphedwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Ndipo Bokosi lachipangano la Chauta lidalandidwa. Ana aŵiri aja a Eli, Hofeni ndi Finehasi, nawonso adaphedwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Ndipo Bokosi la Chipangano la Yehova linalandidwa, ndiponso ana awiri Eli, Hofini ndi Finehasi anaphedwa. Onani mutuwo |