1 Samueli 31:13 - Buku Lopatulika13 Natenga mafupa ao nawaika patsinde pa mtengo wa bwemba uli mu Yabesi, nasala kudya masiku asanu ndi awiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Natenga mafupa ao nawaika patsinde pa mtengo wa bwemba uli m'Yabesi, nasala kudya masiku asanu ndi awiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Pambuyo pake adatenga mafupa ao naŵakwirira patsinde pa mtengo wa mbwemba ku Yabesi, ndipo adasala zakudya masiku asanu ndi aŵiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Pambuyo pake anatenga mafupa awo ndi kuwakwirira pansi pa mtengo wabwemba ku Yabesi, ndipo anasala kudya masiku asanu ndi awiri. Onani mutuwo |