Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 30:28 - Buku Lopatulika

28 ndi kwa iwo a ku Aroere, ndi kwa iwo a ku Sifimoti, ndi kwa iwo a ku Esitemowa;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

28 ndi kwa iwo a ku Aroere, ndi kwa iwo a ku Sifimoti, ndi kwa iwo a ku Esitemowa;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

28 a ku Aroere, a ku Sifimoti, a ku Esitemowa,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

28 Aroeri, Sifimoti, Esitemowa

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 30:28
5 Mawu Ofanana  

Uziya Mwasiterati, Sama ndi Yeiyele ana a Hotamu wa ku Aroere,


ndi woyang'anira minda yampesa ndiye Simei Mramati; ndi woyang'anira zipatso za minda yampesa zisungike mosungiramo vinyo ndiye Zabidi Msifamu;


Malire ao anayambira ku Aroere wokhala m'mphepete mwa chigwa cha Arinoni, ndi mzinda uli pakati pa chigwa ndi chidikha chonse cha ku Medeba;


ndi Anabu, ndi Esitemowa, ndi Animu;


ndi Yatiri ndi mabusa ake, ndi Esitemowa ndi mabusa ake;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa