1 Samueli 30:27 - Buku Lopatulika27 Anatumiza kwa iwo a ku Betele, ndi kwa iwo a ku Ramoti wa kumwera, ndi kwa iwo a ku Yatiri; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Anatumiza kwa iwo a ku Betele, ndi kwa iwo a ku Ramoti wa kumwera, ndi kwa iwo a ku Yatiri; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Mphatsozo zidaperekedwa kwa anthu a ku Betele, a ku Ramoti kumwera kwa Yuda, a ku Yatiri, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Iye anatumiza mphatsozo kwa anthu a ku Beteli, Ramoti-Negavi, Yatiri, Onani mutuwo |