Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 3:5 - Buku Lopatulika

5 Ndipo anathamangira kwa Eli nati, Ndine, popeza mwandiitana ine. Ndipo iye anati, Sindinaitane, kagone. Napita iye, nagona.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Ndipo anathamangira kwa Eli nati, Ndine, popeza mwandiitana ine. Ndipo iye anati, Sindinaitana, kagone. Napita iye, nagona.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Adathamangira kwa Eli nati, “Ndabwera, ndamva kuitana.” Koma Eli adati, “Sindidakuitane, kagone.” Motero Samuele adapita kukagona.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Ndipo iyeyo anathamangira kwa Eli ndipo anati, “Ndabwera ndamva kuyitana.” Koma Eli anati, “Ine sindinakuyitane, bwerera kagone.” Ndipo iye anapita kukagona.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 3:5
2 Mawu Ofanana  

Pamenepo Yehova anaitana Samuele; ndipo iye anayankha kuti, Ndili pano.


Ndipo Yehova anabwereza kumuitana, ndi kuti, Samuele. Ndipo Samuele anauka, napita kwa Eli, nati, Ndine, pakuti mwandiitana ndithu. Koma iye anayankha, Sindinaitane, mwana wanga; kagone.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa