1 Samueli 3:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo kunali nthawi yomweyo Eli atagona m'malo mwake (maso ake anayamba chizirezire osatha kupenya bwino); Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo kunali nthawi yomweyo Eli atagona m'malo mwake (maso ake anayamba chizirezire osatha kupenya bwino); Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Tsiku lina Eli anali gone kumalo kwake. Maso ake adaali atayamba kupenya mwachimbuuzi, kotero kuti sankatha kupenya bwino. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Tsiku lina Eli, amene maso anali ofowoka ndi kuti sankatha kuona bwino, anagona pa malo ake. Onani mutuwo |