1 Samueli 3:2 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Tsiku lina Eli, amene maso anali ofowoka ndi kuti sankatha kuona bwino, anagona pa malo ake. Onani mutuwoBuku Lopatulika2 Ndipo kunali nthawi yomweyo Eli atagona m'malo mwake (maso ake anayamba chizirezire osatha kupenya bwino); Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo kunali nthawi yomweyo Eli atagona m'malo mwake (maso ake anayamba chizirezire osatha kupenya bwino); Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Tsiku lina Eli anali gone kumalo kwake. Maso ake adaali atayamba kupenya mwachimbuuzi, kotero kuti sankatha kupenya bwino. Onani mutuwo |