1 Samueli 29:7 - Buku Lopatulika7 Chifukwa chake, bwerera, numuke mumtendere, kuti angaipidwe mtima nawe akalonga a Afilisti. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Chifukwa chake, bwerera, numuke mumtendere, kuti angaipidwe mtima nawe akalonga a Afilisti. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Choncho ubwerere tsopano. Upite mwamtendere, kuwopa kuti atsogoleri a Afilisti angaipidwe nawe.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Tsono bwerera. Upite mu mtendere kuopa kuti ungachite kanthu kena koyipira atsogoleri a Afilistiwa.” Onani mutuwo |