1 Samueli 29:5 - Buku Lopatulika5 Uyu si Davide kodi amene anamthirirana mang'ombe m'magulu ao, kuti, Saulo anapha zikwi zake, koma Davide zikwi zake zankhani? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Uyu si Davide kodi amene anamthirirana mang'ombe m'magulu ao, kuti, Saulo anapha zikwi zake, koma Davide zikwi zake zankhani? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ameneyutu ndi Davide, yemwe uja ankamuvinira ndi kumuimbira kuti, “ ‘Saulo wapha zikwi inde, koma Davide wapha zikwi khumikhumi?’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Paja ameneyu ndi Davide yemwe ankamuvinira namuyimbira kuti, “ ‘Sauli wapha anthu 1,000 koma Davide wapha miyandamiyanda?’ ” Onani mutuwo |