1 Samueli 28:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo pamene Saulo anaona khamu la Afilisti, anaopa, ndi mtima wake unanjenjemera kwakukulu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo pamene Saulo anaona khamu la Afilisti, anaopa, ndi mtima wake unanjenjemera kwakukulu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Saulo ataona gulu laankhondo la Afilisti, adayamba kuwopa ndi kunjenjemera kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Sauli ataona gulu lankhondo la Afilisti anaopa ndipo ananjenjemera kwambiri. Onani mutuwo |