Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 28:25 - Buku Lopatulika

25 nabwera nazo kwa Saulo ndi kwa anyamata ake; nadya iwowa. Atatero ananyamuka, nachoka usiku womwewo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 nabwera nazo kwa Saulo ndi kwa anyamata ake; nadya iwowa. Atatero ananyamuka, nachoka usiku womwewo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 Tsono adadzapereka bulediyo kwa Saulo ndi nduna zake, ndipo onse adadya. Pambuyo pake adanyamuka, nachokapo usiku womwewo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 Tsono anapereka bulediyo kwa Sauli ndi nduna zake ndipo anadya. Pambuyo pake ananyamuka kupita kwawo usiku womwewo.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 28:25
2 Mawu Ofanana  

Ndipo mkaziyo anali ndi mwanawang'ombe wonenepa m'nyumbamo; ndipo anafulumira, namupha, natenga ufa naukanyanga mkate wopanda chotupitsa;


Tsono Afilisti anasonkhanitsa makamu ao onse ku Afeki; ndipo Aisraele anamanga ku chitsime cha mu Yezireele.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa