1 Samueli 28:24 - Buku Lopatulika24 Ndipo mkaziyo anali ndi mwanawang'ombe wonenepa m'nyumbamo; ndipo anafulumira, namupha, natenga ufa naukanyanga mkate wopanda chotupitsa; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Ndipo mkaziyo anali ndi mwanawang'ombe wonenepa m'nyumbamo; ndipo anafulumira, namupha, natenga ufa naukanyanga mkate wopanda chotupitsa; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Mkaziyo anali ndi mwanawang'ombe wonenepa, ndipo adamupha mwachangu. Adatenga ufa naukanyanga, naphika buledi wosatupitsidwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Mkaziyo anali ndi mwana wangʼombe wonenepa ndipo anamupha mwachangu. Anatenga ufa nawukanyanga ndipo anaphika buledi wopanda yisiti. Onani mutuwo |