1 Samueli 27:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo Akisi anampatsa Zikilagi tsiku lomweli; chifukwa chake Zikilagi ndi wa mafumu a Yuda kufikira lero lomwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo Akisi anampatsa Zikilagi tsiku lomweli; chifukwa chake Zikilagi ndi wa mafumu a Yuda kufikira lero lomwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Choncho tsiku limenelo Akisi adapatsa Davide mudzi wa Zikilagi. Nchifukwa chake mudzi wa Zikilagi ngwa mafumu a Yuda mpaka lero lino. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Choncho tsiku limenelo Akisi anamupatsa Zikilagi ndipo mzindawo wakhala wa mafumu a Yuda mpaka lero. Onani mutuwo |