1 Samueli 25:5 - Buku Lopatulika5 Davide natuma anyamata khumi, nanena kwa anyamatawo, Mukwere ku Karimele, mumuke kwa Nabala ndi kundiperekera moni; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Davide natuma anyamata khumi, nanena kwa anyamatawo, Mukwere ku Karimele, mumuke kwa Nabala ndi kundiperekera moni; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Choncho adatuma anyamata khumi kuti, “Pitani ku phiri la Karimele kwa Nabala, mukandiperekere moni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Choncho anatuma anyamata khumi nawawuza kuti, “Pitani kwa Nabala ku Karimeli ndipo mukamulonjere mʼdzina langa. Onani mutuwo |