1 Samueli 25:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo Davide anamva kuchipululu kuti Nabala alinkusenga nkhosa zake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo Davide anamva kuchipululu kuti Nabala alinkusenga nkhosa zake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Davide anali atamva kuchipululu kuja kuti Nabala akumeta nkhosa zake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Davide anamva akanali ku chipululu kuti Nabala akumeta nkhosa. Onani mutuwo |