Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 25:4 - Buku Lopatulika

4 Ndipo Davide anamva kuchipululu kuti Nabala alinkusenga nkhosa zake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ndipo Davide anamva kuchipululu kuti Nabala alinkusenga nkhosa zake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Davide anali atamva kuchipululu kuja kuti Nabala akumeta nkhosa zake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Davide anamva akanali ku chipululu kuti Nabala akumeta nkhosa.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 25:4
4 Mawu Ofanana  

Ndipo anamuuza Tamara, kuti, Taona, mpongozi wako akwera kunka ku Timna kuti akasenge nkhosa zake.


Ndipo zitapita zaka ziwiri zathunthu, kunali kuti Abisalomu anali nao osenga nkhosa zake ku Baala-Hazori pafupi pa Efuremu; ndipo Abisalomu anaitana ana aamuna onse a mfumu.


Tsono dzina la munthuyo ndiye Nabala, ndi dzina la mkazi wake ndiye Abigaile; ndiye mkazi wa nzeru yabwino, ndi wa nkhope yokongola; koma mwamunayo anali waphunzo ndi woipa machitidwe ake; ndipo iye anali wa banja la Kalebe.


Davide natuma anyamata khumi, nanena kwa anyamatawo, Mukwere ku Karimele, mumuke kwa Nabala ndi kundiperekera moni;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa