1 Samueli 25:44 - Buku Lopatulika44 Pakuti Saulo anapatsa Mikala, mwana wake, mkazi wa Davide, kwa Paliti mwana wa Laisi, wa ku Galimu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201444 Pakuti Saulo anapatsa Mikala, mwana wake, mkazi wa Davide, kwa Paliti mwana wa Laisi, wa ku Galimu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa44 Paja Saulo anali atakwatitsa mwana wake Mikala, mkazi wa Davide, kwa Paliti mwana wa Laisi wa ku Galimu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero44 Koma Sauli anali atakwatitsa Mikala, mkazi wa Davide kwa Paliti mwana wa Laisi wa ku Galimu. Onani mutuwo |