Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Samueli 25:43 - Buku Lopatulika

43 Davide anatenganso Ahinowamu wa ku Yezireele, ndipo onse awiri anakhala akazi ake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

43 Davide anatenganso Ahinowamu wa ku Yezireele, ndipo onse awiri anakhala akazi ake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

43 Davide anali atakwatira Ahinowamu wa ku Yezireele, ndipo aŵiri onsewo adakhala akazi ake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

43 Davide nʼkuti atakwatiranso Ahinoamu wa ku Yezireeli ndipo onse awiri anali akazi ake.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 25:43
10 Mawu Ofanana  

Chifukwa chotero mwamuna adzasiya atate wake ndi amake nadzadziphatika kwa mkazi wake: ndipo adzakhala thupi limodzi.


Chomwecho Davide anakwera kunka kumeneko pamodzi ndi akazi ake awiri, ndiwo Ahinowamu Myezireele, ndi Abigaile mkazi wa Nabala wa ku Karimele.


Ndipo ana a Davide anabadwira ku Hebroni. Mwana woyamba ndiye Aminoni, wa Ahinowamu wa ku Yezireele;


nati, Chifukwa cha ichi mwamuna adzasiya atate wake ndi amake, nadzaphatikizana ndi mkazi wake, ndipo awiriwo adzakhala thupi limodzi?


Iye ananena kwa iwo, Chifukwa cha kuuma mtima kwanu, Mose anakulolezani kuchotsa akazi anu; koma pachiyambi sikunakhala chomwecho.


ndi Yezireele, ndi Yokodeamu, ndi Zanowa;


Ndipo Davide anakhala ndi Akisi ku Gati, iye ndi anthu ake, munthu yense ndi a pabanja pake, inde Davide ndi akazi ake awiri, Ahinowamu wa ku Yezireele, ndi Abigaile wa ku Karimele, mkazi wa Nabala.


Chomwecho Davide analawirira, iye ndi anthu ake, kuti amuke m'mawa ndi kubwera ku dziko la Afilisti. Ndipo Afilisti anakwera Yezireele.


Ndipo akazi awiri a Davide anatengedwa ukapolo, Ahinowamu wa ku Yezireele ndi Abigaile mkazi wa Nabala wa ku Karimele.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa