Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 26:1 - Buku Lopatulika

1 Ndipo Azifi anafika kwa Saulo ku Gibea, nati, Kodi Davide sali kubisala m'phiri la Hakila, kupenya kuchipululu!

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndipo Azifi anafika kwa Saulo ku Gibea, nati, Kodi Davide sali kubisala m'phiri la Hakila, kupenya kuchipululu!

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Tsiku lina anthu a ku Zifi adabwera kwa Saulo ku Gibea, namuuza kuti, “Davide akubisala ku phiri la Hakila limene lili kuvuma kwa Yesimoni.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Anthu a ku Zifi anapita kwa Sauli ku Gibeya nati, “Davide akubisala ku phiri la Hakila, limene limayangʼanana ndi Yesimoni.”

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 26:1
5 Mawu Ofanana  

Zifi ndi Telemu ndi Bealoti;


Maoni, Karimele, ndi Zifi, ndi Yuta;


Ndipo a ku Zifi anakwera kwa Saulo ku Gibea, nati, Davide salikubisala kwathu kodi, m'ngaka za m'nkhalango ku Horesi, m'phiri la Hakila, limene lili kumwera kwa chipululu?


Saulo namanga zithando m'phiri la Hakila kupenya kuchipululu kunjira. Koma Davide anakhala kuchipululu, naona kuti Saulo alikumfuna kuchipululu komweko.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa