1 Samueli 25:30 - Buku Lopatulika30 Ndipo kudzali, pamene Yehova anachitira mbuye wanga monga mwa zabwino zonse adalankhula za inu, ndipo adadzaika inu mukhale kalonga wa Israele; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Ndipo kudzali, pamene Yehova anachitira mbuye wanga monga mwa zabwino zonse adalankhula za inu, ndipo adadzaika inu mukhale kalonga wa Israele; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Inu mbuyanga, Chauta adzakuchitirani zabwino zonse zimene adakulonjezani, ndipo adzakuikani kuti mukhale mfumu yolamulira Aisraele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Yehova adzakuchitirani mbuye wanga zabwino zonse zimene anakulonjezani. Adzakuyikani kukhala wolamulira Aisraeli. Onani mutuwo |