1 Samueli 25:29 - Buku Lopatulika29 Ngakhale anauka anthu kukulondolani, ndi kufuna moyo wanu, koma moyo wa mbuye wanga udzamangika m'phukusi la amoyo lakukhala ndi Yehova Mulungu wanu; koma Iye adzaponya miyoyo ya adani anu kuwataya monga chotuluka m'choponyera mwala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Ngakhale anauka anthu kukulondolani, ndi kufuna moyo wanu, koma moyo wa mbuye wanga udzamangika m'phukusi la amoyo lakukhala ndi Yehova Mulungu wanu; koma Iye adzaponya miyoyo ya adani anu kuwataya monga chotuluka m'choponyera mwala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Ngati anthu akuukirani namakulondolani kuti akupheni, Chauta Mulungu wanu adzakusungani, monga m'mene munthu amasungira chuma m'phukusi. Koma moyo wa adani anu, Iye adzautaya kutali, monga m'mene munthu amaponyera mwala ndi khwenengwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Ngati munthu wina akuwukirani ndi kukulondani, Yehova Mulungu wanu adzateteza moyo wa mbuye wanga monga mmene munthu asungira chuma mʼphukusi, koma moyo wa adani anu adzawutaya kutali monga momwe munthu amaponyera mwala ndi legeni. Onani mutuwo |