Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 25:20 - Buku Lopatulika

20 Ndipo kudatero pakuberekeka iye pabulu wake, natsikira pamalo obisika a m'phirilo, onani, Davide ndi anthu ake analikutsikira kwa iye; iye nakomana nao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Ndipo kudatero pakuberekeka iye pa bulu wake, natsikira pa malo obisika a m'phirilo, onani, Davide ndi anthu ake analikutsikira kwa iye; iye nakomana nao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Tsono mkaziyo atakwera pa bulu ndi kufika patsinde pa phiri lina, adangoona Davide ndi ankhondo ake akubwera kwa iye. Ndipo mkaziyo adakumana nawo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Mayi uja atakwera pa bulu wake ndi kufika pa tsinde la phiri, anangoona Davide ndi ankhondo ake akubwera kunali iye. Choncho anakumana nawo.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 25:20
3 Mawu Ofanana  

Pamenepo anamangirira bulu mbereko, nati kwa mnyamata wake, Kusa, tiye; usandilezetsa kuyendaku, ndikapanda kukuuza.


Nati kwa anyamata ake, Nditsogolereni; onani ndidza m'mbuyo mwanu. Koma sanauze mwamuna wake Nabala.


Koma Davide adanena, Zoonadi ndasunga chabe zake zonse za kaja kanali nazo m'chipululu, sikadasowe kanthu ka zake zonse; ndipo iye anandibwezera zoipa m'malo mwa zabwino.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa