1 Samueli 25:19 - Buku Lopatulika19 Nati kwa anyamata ake, Nditsogolereni; onani ndidza m'mbuyo mwanu. Koma sanauze mwamuna wake Nabala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Nati kwa anyamata ake, Nditsogolereni; onani ndidza m'mbuyo mwanu. Koma sanauze mwamuna wake Nabala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Kenaka adauza anyamata ake antchito kuti, “Batsogolani, ine ndikudza pambuyo panu.” Koma sadauze Nabala mwamuna wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Kenaka anawuza antchito ake kuti, “Tsogolani, ine ndikutsatirani.” Koma sanawuze mwamuna wake Nabala. Onani mutuwo |