1 Samueli 25:10 - Buku Lopatulika10 Koma Nabala anayankha anyamata a Davide nati, Davide ndani? Ndi mwana wa Yese ndani? Masiku ano pali anyamata ambiri akungotaya ambuye ao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Koma Nabala anayankha anyamata a Davide nati, Davide ndani? Ndi mwana wa Yese ndani? Makono ano pali anyamata ambiri akungotaya ambuye ao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Nabala adayankha anyamata a Davide aja poŵafunsa kuti, “Kodi Davide mwana wa Yese ndani? Ha! Masiku ano pali anthu antchito ambiri amene akuthaŵa kwa ambuyao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Nabala anayankha anyamata a Davide kuti, “Kodi Davide ndi ndani? Mwana wa Yese ndi ndani? Masiku ano pali antchito ambiri amene akuthawa kwa mabwana awo. Onani mutuwo |