1 Samueli 23:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo kunali kuti Abiyatara mwana wa Ahimeleki pakuthawira kwa Davide ku Keila, anatsika ali ndi efodi m'dzanja lake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo kunali kuti Abiyatara mwana wa Ahimeleki pakuthawira kwa Davide ku Keila, anatsika ali ndi efodi m'dzanja lake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Pamene Abiyatara, mwana wa Ahimeleki, adathaŵira kwa Davide ku Keila, adabwera atatenga efodi yaunsembe ija m'manja mwake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 (Pamene Abiatara mwana wa Ahimeleki anathawira kwa Davide anabwera ndi efodi mʼmanja mwake). Onani mutuwo |