1 Samueli 23:20 - Buku Lopatulika20 Chifukwa chake mfumu, tsikani, monga umo mukhumbire m'mtima mwanu kutsika; ndipo kudzakhala kwathu kumpereka iye m'dzanja la mfumu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Chifukwa chake mfumu, tsikani, monga umo mukhumbire m'mtima mwanu kutsika; ndipo kudzakhala kwathu kumpereka iye m'dzanja la mfumu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Tsono inu amfumu, ife tadziŵa kuti mukumfunafuna kwambiri, choncho bwerani ndithu. Ifeyo tidzampereka kwa inu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Tsopano inu, mubwere nthawi iliyonse imene mukufuna, ndipo ife tidzamupereka kwa mfumu.” Onani mutuwo |