1 Samueli 23:2 - Buku Lopatulika2 Chifukwa chake Davide anafunsira kwa Yehova, nati, Ndimuke kodi kukakantha Afilisti aja? Ndipo Yehova anati kwa Davide, Muka, nukanthe Afilisti, ndi kupulumutsa Keila. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Chifukwa chake Davide anafunsira kwa Yehova, nati, Ndimuke kodi kukakantha Afilisti aja? Ndipo Yehova anati kwa Davide, Muka, nukanthe Afilisti, ndi kupulumutsa Keila. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Choncho Davide adafunsa Chauta kuti, “Kodi ndikamenyane nawo nkhondo Afilistiwo?” Chauta adamuuza kuti, “Pita, kamenyane nawo, kuti upulumutse mzinda wa Keila.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 anafunsa Yehova kuti, “Kodi ndipite ndikamenyane nawo Afilistiwa?” Yehova anamuyankha kuti, “Pita, kamenyane nawo Afilisti ndi kupulumutsa mzinda wa Keila.” Onani mutuwo |