1 Samueli 23:17 - Buku Lopatulika17 Ndipo iye ananena naye, Usaopa; chifukwa dzanja la Saulo atate wanga silidzakupeza; iwe udzakhala mfumu ya Israele, ndipo ine ndidzakhala wotsatana nawe, ichinso Saulo atate wanga achidziwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndipo iye ananena naye, Usaopa; chifukwa dzanja la Saulo atate wanga silidzakupeza; iwe udzakhala mfumu ya Israele, ndipo ine ndidzakhala wotsatana nawe, ichinso Saulo atate wanga achidziwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Yonatani adauza Davide kuti, “Usaope, abambo anga sadzakupha. Udzakhala mfumu ya Aisraele, ndipo ine ndidzakhala wachiŵiri kwa iwe. Abambo angawo akudziŵanso zimenezi.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Iye anamuwuza kuti, “Usaope, abambo anga sadzakupha. Iwe udzakhala mfumu ya Israeli ndipo ine ndidzakhala wachiwiri wako. Ngakhale abambo anga Sauli akudziwa zimenezi.” Onani mutuwo |