1 Samueli 23:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo Yonatani mwana wa Saulo ananyamuka, napita kwa Davide kunkhalangoko, namlimbitsa dzanja lake mwa Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo Yonatani mwana wa Saulo ananyamuka, napita kwa Davide kunkhalangoko, namlimbitsa dzanja lake mwa Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Tsono Yonatani, mwana wa Saulo, adanyamuka napita kwa Davide ku Horesi, ndipo adamlimbitsa mtima pomuuza kuti Mulungu adzamteteza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Ndipo Yonatani mwana wa Sauli anapita kwa Davide ku Horesi ndipo anamulimbitsa mtima pomuwuza kuti Yehova ali naye. Onani mutuwo |