Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 22:9 - Buku Lopatulika

9 Pamenepo Doegi wa ku Edomu, anaimirira ndi anyamata a Saulo, nayankha, nati, Ine ndinamuona mwana wa Yeseyo alikufika ku Nobu, kwa Ahimeleki mwana wa Ahitubi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Pamenepo Doegi wa ku Edomu, anaimirira ndi anyamata a Saulo, nayankha, nati, Ine ndinamuona mwana wa Yeseyo alikufika ku Nobu, kwa Ahimeleki mwana wa Ahitubi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Apo Doegi Mwedomu, amene adaaimirira pafupi ndi nduna za Saulo, adanena kuti, “Ine ndidamuwona mwana wa Yese akupita ku Nobu kwa Ahimeleki, mwana wa Ahitubi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Koma Doegi Mwedomu anayima pafupi ndi nduna za Sauli nati, “Ine ndinaona mwana wa Yese atabwera kwa Ahimeleki mwana wa Ahitubi ku Nobi.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 22:9
8 Mawu Ofanana  

Mboni yonama sidzakhala yosalangidwa; wolankhula mabodza sadzapulumuka.


Mkulu akamvera chinyengo, atumiki ake onse ali oipa.


Lero lomwe adzaima pa Nobu; agwedezera dzanja lake paphiri la mwana wamkazi wa Ziyoni, phiri la Yerusalemu.


Anthu oneneza anali mwa iwe, kuti akhetse mwazi; ndipo anadya pamapiri mwa iwe, pakati pa iwe anachita zamanyazi.


ndi Ahiya mwana wa Ahitubi mbale wake wa Ikabodi, mwana wa Finehasi, mwana wa Eli, wansembe wa Yehova wa ku Silo, wovala efodi. Ndipo anthuwo sanadziwe kuti Yonatani wachoka.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa