1 Samueli 22:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo iye anamfunsira kwa Yehova, nampatsa chakudya, nampatsanso lupanga la Goliyati Mfilistiyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo iye anamfunsira kwa Yehova, nampatsa chakudya, nampatsanso lupanga la Goliyati Mfilistiyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Ndipo Ahimelekiyo adafunsa Chauta zimene Davide ankayenera kuchita. Kenaka adampatsa chakudya, nampatsanso lupanga la Goliyati, Mfilisti uja.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Ahimelekiyo anafunsa kwa Yehova chomwe Davide ayenera kuchita. Iye anamupatsa zakudya ndiponso lupanga la Goliati Mfilisiti uja.” Onani mutuwo |