1 Samueli 22:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo yense wosautsidwa, ndi yense wa ngongole, ndi yense wowawidwa mtima, anaunjikana kwa iye; iye nakhala mtsogoleri wao; ndipo anali nao anthu ngati mazana anai. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo yense wosautsidwa, ndi yense wa ngongole, ndi yense wowawidwa mtima, anaunjikana kwa iye; iye nakhala mtsogoleri wao; ndipo anali nao anthu ngati mazana anai. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Tsono aliyense amene anali pa mavuto, kapena anali ndi ngongole, kapena anali wosakondwa, onsewo adasonkhana kwa Davide. Iyeyo ankaŵatsogolera. Onse anali ngati anthu 400 pamodzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ndipo aliyense amene anali pa mavuto, kapena ndi ngongole kapenanso amene anali wosakondwa anasonkhana kwa iye, ndipo iye anakhala mtsogoleri wawo. Onse pamodzi analipo amuna 400. Onani mutuwo |