1 Samueli 22:14 - Buku Lopatulika14 Ndipo Ahimeleki anayankha mfumu, nati, Ndipo ndani mwa anyamata anu onse ali wokhulupirika ngati Davide amene, mkamwini wa mfumu; wakuyenda mu uphungu wanu, nalemekezeka m'nyumba mwanu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndipo Ahimeleki anayankha mfumu, nati, Ndipo ndani mwa anyamata anu onse ali wokhulupirika ngati Davide amene, mkamwini wa mfumu; wakuyenda mu uphungu wanu, nalemekezeka m'nyumba mwanu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Koma Ahimeleki adayankha mofunsa kuti, “Amfumu, kodi ndani pakati pa ankhondo anu amene ali wokhulupirika ngati Davide? Iye uja ndi mkamwini wanu, mtsogoleri wa gulu lanu lokutchinjirizani, ndiponso munthu wolemekezeka m'banja mwanu? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Ahimeleki anayankha mfumu kuti, “Kodi ndani mwa ankhondo anu onse amene ali wokhulupirika monga Davide? Iye uja ndi mkamwini wa mfumu, kapitawo wa asilikali okutetezani ndiponso munthu amene amalemekezedwa mʼbanja lanu? Onani mutuwo |