Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 21:15 - Buku Lopatulika

15 Kodi ndisowa anthu amisala kuti mwabwera ndi uyu kuti akhale wamisala pamaso panga? Kodi uyu adzalowa m'nyumba mwanga?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Kodi ndisowa anthu amisala kuti mwabwera ndi uyu kuti akhale wamisala pamaso panga? Kodi uyu adzalowa m'nyumba mwanga?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Kodi ndikusoŵa anthu amisala kuti muzibwera naye kuno munthu ameneyu, namachita zamisala zake pamaso panga? Ha! Munthu wotereyu angaloŵe bwanji m'nyumba mwanga muno?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Kodi ine ndikusowa anthu amisala kuti muzibwera naye munthuyu kwa ine kuti azidzachita zamisala zake pamaso panga? Kodi munthu ameneyu nʼkulowa mʼnyumba mwanga?”

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 21:15
3 Mawu Ofanana  

Nduna zinandilondola kopanda chifukwa; koma mtima wanga uchita nao mantha mau anu.


Tsono Akisi ananena ndi anyamata ake, Taonani, mupenya kuti munthuyo ngwa misala; mwabwera naye kwa ine chifukwa ninji?


Motero Davide anachoka kumeneko, napulumukira ku phanga la ku Adulamu; ndipo pamene abale ake ndi banja lonse la atate wake anamva, iwo anatsikira kumeneko kwa iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa