1 Samueli 21:14 - Buku Lopatulika14 Tsono Akisi ananena ndi anyamata ake, Taonani, mupenya kuti munthuyo ngwa misala; mwabwera naye kwa ine chifukwa ninji? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Tsono Akisi ananena ndi anyamata ake, Taonani, mupenya kuti munthuyo ngwa misala; mwabwera naye kwa ine chifukwa ninji? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Tsono Akisi adauza nduna zake kuti, “Mukuwona kuti munthuyu ngwamisala. Chifukwa chiyani tsono mwabwera naye kwa ine? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Akisi anawuza nduna zake kuti, “Mukumuona munthu uyu kuti ndi wamisala! Nʼchifukwa chiyani mukubwera naye kwa ine? Onani mutuwo |