Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 21:14 - Buku Lopatulika

14 Tsono Akisi ananena ndi anyamata ake, Taonani, mupenya kuti munthuyo ngwa misala; mwabwera naye kwa ine chifukwa ninji?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Tsono Akisi ananena ndi anyamata ake, Taonani, mupenya kuti munthuyo ngwa misala; mwabwera naye kwa ine chifukwa ninji?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Tsono Akisi adauza nduna zake kuti, “Mukuwona kuti munthuyu ngwamisala. Chifukwa chiyani tsono mwabwera naye kwa ine?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Akisi anawuza nduna zake kuti, “Mukumuona munthu uyu kuti ndi wamisala! Nʼchifukwa chiyani mukubwera naye kwa ine?

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 21:14
4 Mawu Ofanana  

Ndidzalemekeza Yehova nyengo zonse; kumlemekeza kwake kudzakhala m'kamwa mwanga kosalekeza.


Indetu nsautso uyalutsa wanzeru; ndi mtulo uipitsa mtima.


Nasanduliza makhalidwe ake pamaso pao, nadzionetsera m'manja mwao ngati wamisala, nangolembalemba pa zitseko za chipata, nakhetsa dovu lake pa ndevu yake.


Kodi ndisowa anthu amisala kuti mwabwera ndi uyu kuti akhale wamisala pamaso panga? Kodi uyu adzalowa m'nyumba mwanga?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa