Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 20:39 - Buku Lopatulika

39 Koma mnyamatayo sanadziwe kanthu; Davide ndi Yonatani okha anadziwa za mlanduwo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

39 Koma mnyamatayo sanadziwe kanthu; Davide ndi Yonatani okha anadziwa za mlanduwo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

39 Koma mnyamatayo sadadziŵe kanthu ai, Yonatani yekha ndi Davide ndiwo amene ankadziŵa zimene zinkachitika.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

39 (Mnyamatayo sanadziwe chimene chimachitika koma Yonatani ndi Davide ndiwo ankadziwa).

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 20:39
2 Mawu Ofanana  

Ndipo Yonatani anafuulira mnyamatayo, nati, Yendetsa, fulumira, usaima. Ndi mnyamata wa Yonatani anatola mivi, nafika kwa mbuye wake.


Ndipo Yonatani anapatsa mnyamata wake zida zake, nanena naye, Muka, tenga izi kunka nazo kumzinda.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa