Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 20:40 - Buku Lopatulika

40 Ndipo Yonatani anapatsa mnyamata wake zida zake, nanena naye, Muka, tenga izi kunka nazo kumzinda.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

40 Ndipo Yonatani anapatsa mnyamata wake zida zake, nanena naye, Muka, tenga izi kunka nazo kumudzi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

40 Choncho Yonatani adapereka zida zake kwa mnyamata wake uja, namuuza kuti, “Pita, kazitule ku mzinda.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

40 Pambuyo pake Yonatani anapereka zida zake za nkhondo kwa mnyamatayo ndipo anati, “Pita, nyamula ubwerere nazo ku mzinda.”

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 20:40
2 Mawu Ofanana  

Koma mnyamatayo sanadziwe kanthu; Davide ndi Yonatani okha anadziwa za mlanduwo.


Pomwepo pochoka mnyamatayo, Davide, anauka chakumwera, nagwa nkhope yake pansi, nawerama katatu; ndipo iwowa anapsompsonana, nalirirana, kufikira Davide analiritsa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa