Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 20:38 - Buku Lopatulika

38 Ndipo Yonatani anafuulira mnyamatayo, nati, Yendetsa, fulumira, usaima. Ndi mnyamata wa Yonatani anatola mivi, nafika kwa mbuye wake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

38 Ndipo Yonatani anafuulira mnyamatayo, nati, Yendetsa, fulumira, usaima. Ndi mnyamata wa Yonatani anatola mivi, nafika kwa mbuye wake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

38 Apo Yonatani adaitananso mnyamatayo nati, “Fulumira, yenda msanga, usachedwe.” Motero mnyamata uja adatola muviwo, nabwera kwa mbuyake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

38 Yonatani anayitananso mnyamatayo kuti, “Fulumira, pita msanga usayime.” Choncho mnyamatayo anatola muvi uja ndi kubwera nayo kwa mbuye wake.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 20:38
7 Mawu Ofanana  

Ndipo mnyamatayo atafika pamalo a muvi umene Yonatani anauponya, Yonatani anafuulira mnyamatayo, nati, Muviwo suli m'tsogolo mwako kodi?


Koma mnyamatayo sanadziwe kanthu; Davide ndi Yonatani okha anadziwa za mlanduwo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa